Yeremiya 7:29 - Buku Lopatulika29 Meta tsitsi lako, iwe Yerusalemu, nulitaye, nukweze maliro pa mapiri oti see; pakuti Yehova wakana ndi kusiya mbadwo umene aukwiyira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Meta tsitsi lako, iwe Yerusalemu, nulitaye, nukweze maliro pa mapiri oti see; pakuti Yehova wakana ndi kusiya mbadwo umene aukwiyira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 “Meta tsitsi lako, ndipo ulitaye. Ulire kwambiri pa zitunda zopanda zomera, poti Chauta waukana mbadwo uwu umene wamkwiyitsa. Anthu amenewo Iye waŵasiyadi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 “Tsono meta tsitsi lako ndi kulitaya. Ulire kwambiri pa zitunda zopanda zomera, pakuti Yehova waukana ndi kuwusiya mʼbado umene wamukwiyitsawu.” Onani mutuwo |