Yeremiya 7:26 - Buku Lopatulika26 koma sanandimvere Ine sanatchere khutu lao, koma anaumitsa khosi lao; anaipa koposa makolo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 koma sanandimvere Ine sanatchera khutu lao, koma anaumitsa khosi lao; anaipa koposa makolo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Komabe inu simudandimvere, simudasamaleko. Ndi mitima yanu yokanika, mwaipa kupambana makolo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Koma anthuwo sanandimvere kapena kusamalira. Anawumitsa mitima yawo ndi kuchita zoyipa kuposa makolo awo. Onani mutuwo |