Yeremiya 7:19 - Buku Lopatulika19 Kodi autsa mkwiyo wanga? Ati Yehova; kodi sadziutsira okha manyazi a nkhope zao? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Kodi autsa mkwiyo wanga? Ati Yehova; kodi sadziutsira okha manyazi a nkhope zao? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Amati atani! Amayesa kuti akuvuta Ine, koma akungodzivuta okha ndi kumadzichititsa manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma kodi akuvutitsa Ine? Kodi sakungodzivuta okha, ndi kudzichititsa manyazi? akutero Yehova.” Onani mutuwo |