Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 6:5 - Buku Lopatulika

5 Ukani, tiyende usiku, tipasule nyumba zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ukani, tiyende usiku, tipasule nyumba zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 “Bwerani tsono tiwuthire nkhondo usiku uno, tiwononge malinga ake.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Tsono nyamukani kuti tiwuthire nkhondo mzindawu usiku uno ndi kuwononga malinga ake!”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 6:5
12 Mawu Ofanana  

Ndipo anatentha nyumba ya Mulungu, nagumula linga la Yerusalemu, natentha nyumba zake zonse zachifumu ndi moto, naononga zipangizo zake zonse zokoma.


Mulungu adziwika m'zinyumba zake ngati msanje.


pakuti nyumba ya mfumu idzasiyidwa; mzinda wa anthu ambiri udzakhala bwinja; chitunda ndi nsanja zidzakhala nkhwimba kunthawi zonse, pokondwera mbidzi podyera zoweta;


Koma ngati simudzamvera Ine kulipatula tsiku la Sabata, kusanyamula katundu ndi kulowa pa zipata za Yerusalemu tsiku la Sabata; pamenepo ndidzayatsa moto m'zipata zakezo, ndipo udzatha zinyumba za Yerusalemu, osazimidwanso.


ndipo anatentha nyumba ya Yehova ndi nyumba ya mfumu, ndi nyumba zonse za mu Yerusalemu, ngakhale zinyumba zazikulu zonse, anazitentha ndi moto.


Pamenepo anaboola mzinda, ndipo anathawa amuna onse a nkhondo, natuluka m'mzinda usiku panjira ya kuchipata cha pakati pa makoma awiri, imene inali pamunda wa mfumu; Ababiloni alikumenyana ndi mzinda pozungulira pake, ndipo anapita njira ya kuchidikha.


Pakuti imfa yakwera m'mazenera athu, yalowa m'nyumba mwathu; kuchotsa ana kubwalo, ndi anyamata kumiseu.


Pakuti Israele waiwala Mlengi wake, namanga akachisi; ndipo Yuda wachulukitsa mizinda yamalinga; koma ndidzatumizira mizinda yake moto, nudzatha nyumba zake zazikulu.


koma ndidzatumiza moto pa Yuda, udzanyeketsa nyumba zachifumu za mu Yerusalemu.


Masomphenya a Obadiya. Atero Ambuye Yehova za Edomu: Tamva mbiri yochokera kwa Yehova, ndi mthenga wotumidwa mwa amitundu, ndi kuti, Nyamukani, timuukire kumthira nkhondo.


Tsegula pa makomo ako Lebanoni, kuti moto uthe mikungudza yako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa