Yeremiya 6:25 - Buku Lopatulika25 Usatulukire kumunda, usayenda m'njira; pakuti lupanga la amaliwongo ndi mantha ali m'mbali zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Usatulukire kumunda, usayenda m'njira; pakuti lupanga la amaliwongo ndi mantha ali m'mbali zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Musayesere kupita ku minda, kapena kuyenda pa mseu, pakuti adani akubwera ndi nkhondo ndipo ponseponse pali mantha okhaokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Musapite ku minda kapena kuyenda mʼmisewu, pakuti mdani ali ndi lupanga, ndipo ponseponse anthu akuchita mantha. Onani mutuwo |