Yeremiya 6:20 - Buku Lopatulika20 Lubani andifumiranji ku Sheba, ndi nzimbe ku dziko lakutali? Nsembe zopsereza zanu sizindisekeretsa, nsembe zophera zanu sizindikondweretsa Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Lubani andifumiranji ku Sheba, ndi nzimbe ku dziko lakutali? Nsembe zopsereza zanu sizindisekeretsa, nsembe zophera zanu sizindikondweretsa Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Kodi pali phindu lanji kwa Ine, ngakhale abwere ndi lubani kuchokera ku Sheba, kapena zonunkhira zina kuchokera ku maiko akutali? Sindidzalandira zopereka zao zopsereza, nsembe zao sizindikondwetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Kodi pali phindu lanji ngakhale mubwere ndi lubani kuchokera ku Seba, kapena zonunkhira zina kuchokera ku dziko lakutali? Nsembe zanu zopsereza Ine sindidzalandira; nsembe zanu sizindikondweretsa.” Onani mutuwo |