Yeremiya 6:18 - Buku Lopatulika18 Chifukwa chake tamverani, amitundu inu, dziwani, msonkhano inu, chimene chili mwa iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Chifukwa chake tamverani, amitundu inu, dziwani, msonkhano inu, chimene chili mwa iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nchifukwa chake imvani inu anthu a mitundu ina, penyetsetsani, inu mwasonkhana panonu, zimene zidzaŵagwere anthuwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nʼchifukwa chake imvani, inu anthu a mitundu ina; yangʼanitsitsani, inu amene mwasonkhana pano, chimene chidzawachitikire anthuwo. Onani mutuwo |