Yeremiya 6:14 - Buku Lopatulika14 Ndiponso apoletsa bala la anthu anga pang'onong'ono, ndi kuti, Mtendere, mtendere; koma palibe mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndiponso apoletsa bala la anthu anga pang'onong'ono, ndi kuti, Mtendere, mtendere; koma palibe mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Iwo amapoletsa mabala a anthu anga pamwamba pokha. Amangonena kuti, ‘Kuli mtendere, kuli mtendere,’ chonsecho kulibe konse mtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Amapoletsa zilonda za anthu anga pamwamba pokha. Iwo amanena kuti, ‘Mtendere, mtendere,’ pamene palibe mtendere. Onani mutuwo |