Yeremiya 6:12 - Buku Lopatulika12 Nyumba zao zidzasanduka za ena, pamodzi ndi minda yao ndi akazi ao; pakuti ndidzatambasula dzanja langa pa okhala m'dziko, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Nyumba zao zidzasanduka za ena, pamodzi ndi minda yao ndi akazi ao; pakuti ndidzatambasula dzanja langa pa okhala m'dziko, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nyumba zao zidzapatsidwa kwa ena pamodzi ndi minda yao ndi akazi ao omwe. Ndithuditu, ndi dzanja langali ndidzakantha anthu okhala m'dzikomo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Nyumba zawo adzazipereka kwa ena, pamodzi ndi minda yawo ndi akazi awo. Ndidzatambasula dzanja langa kukantha anthu okhala mʼdzikomo,” akutero Yehova. Onani mutuwo |