Yeremiya 6:10 - Buku Lopatulika10 Ndidzanena ndi yani, ndidzachita mboni kwa yani, kuti amve? Taona khutu lao lili losadulidwa, ndipo sangathe kumva; taona, mau a Yehova awatonzetsa iwo; sakondwera nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndidzanena ndi yani, ndidzachita mboni kwa yani, kuti amve? Taona khutu lao lili losadulidwa, ndipo sangathe kumva; taona, mau a Yehova awatonzetsa iwo; sakondwera nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kodi ndilankhule ndi yani, ndipo ndichenjeze yani, kuti amve? Makutu ao ndi otsekeka, sangathe kumva. Mau a Chauta amaŵanyoza kwambiri, saŵalabadira konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kodi ndiyankhule ndi yani ndi kumuchenjeza? Ndinene mawu ochenjeza kwa yani kuti amve? Makutu awo ndi otsekeka kotero kuti sangathe kumva. Mawu a Yehova ndi onyansa kwa iwo; sasangalatsidwa nawo. Onani mutuwo |