Yeremiya 52:6 - Buku Lopatulika6 Mwezi wachinai, tsiku lachisanu ndi chinai la mwezi, njala inavuta m'mzinda, ndipo anthu a m'dziko analibe zakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mwezi wachinai, tsiku lachisanu ndi chinai la mwezi, njala inavuta m'mudzi, ndipo anthu a m'dziko analibe zakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono pa tsiku lachisanu ndi chinai, pa mwezi wachinai wa chaka chimenecho, pamene njala inali itakula kwambiri mumzindamo kotero kuti anthu analibiretu chakudya m'dzikomo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pa tsiku lachisanu ndi chinayi la mwezi wachinayi njala inakula kwambiri mu mzindamo kotero kuti munalibe chakudya choti anthu nʼkudya. Onani mutuwo |