Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 52:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo mzinda unazingidwa mpaka chaka cha khumi ndi chimodzi cha mfumu Zedekiya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo mudzi unazingidwa mpaka chaka cha khumi ndi chimodzi cha mfumu Zedekiya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Motero mzindawo udaazingidwa ndi zithandozo mpaka chaka cha 11 cha ufumu wa Zedekiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mzindawo unazingidwa mpaka chaka cha khumi ndi chimodzi cha ulamuliro wa Mfumu Zedekiya.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 52:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mzindawo unazingidwa ndi timalinga mpaka chaka chakhumi ndi chimodzi cha mfumu Zedekiya.


Ndipo kunali chaka chakhumi ndi chimodzi, mwezi wachitatu, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa