Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 52:34 - Buku Lopatulika

34 Koma phoso lake mfumu ya ku Babiloni sanaleke kumpatsa, phoso tsiku ndi tsiku gawo lake, mpaka tsiku la kufa kwake, masiku onse a moyo wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Koma phoso lake mfumu ya ku Babiloni sanaleke kumpatsa, phoso tsiku ndi tsiku gawo lake, mpaka tsiku la kufa kwake, masiku onse a moyo wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Kunena za phoso, mfumu ya ku Babiloni inkampatsa Yehoyakimu phoso lake tsiku ndi tsiku mpaka kufa kwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Tsiku ndi tsiku mfumu ya ku Babuloni inkamupatsa Yehoyakini phoso lake nthawi yonse ya moyo wake, mpaka pa nthawi ya imfa yake.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 52:34
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uzimlimira munda wake, iwe ndi ana ako ndi anyamata ako; nuzibwera nazo zipatso zake kuti mwana wa mbuye wako akhale ndi zakudya; koma Mefiboseti, mwana wa mbuye wako, adzadya pa gome langa masiku onse. Ndipo Ziba anali nao ana aamuna khumi ndi asanu, ndi anyamata makumi awiri.


Ndi kunena za chakudya chake, panali chakudya chosalekeza chopatsidwa kwa iye ndi mfumu, tsiku lililonse gawo lake, masiku onse a moyo wake.


Tsono asanabwerere iye anati, Bweratu kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu, mwana wa Safani, amene mfumu ya ku Babiloni inamyesa wolamulira mizinda ya Yuda, nukhale naye pakati pa anthu; kapena pita kulikonse ukuyesa koyenera kupitako. Ndipo kapitao wa alonda anampatsa iye phoso ndi mtulo, namleka amuke.


Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero.


tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa