Yeremiya 52:30 - Buku Lopatulika30 chaka cha makumi awiri ndi zitatu cha Nebukadinezara Nebuzaradani kapitao wa alonda anatenga ndende Ayuda mazana asanu ndi awiri kudza makumi anai ndi asanu; anthu onse anali zikwi zinai kudza mazana asanu ndi limodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 chaka cha makumi awiri ndi zitatu cha Nebukadinezara Nebuzaradani kapitao wa alonda anatenga ndende Ayuda mazana asanu ndi awiri kudza makumi anai ndi asanu; anthu onse anali zikwi zinai kudza mazana asanu ndi limodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Pa chaka cha 23 cha ufumu wa Nebukadinezara, Nebuzaradani mtsogoleri wa alonda oteteza mfumu uja adatenga ukapolo Ayuda 745. Onse pamodzi otengedwa ukapolo adakwanira 4,600. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 mʼchaka cha 23 cha ulamuliro wa Nebukadinezara, Nebuzaradani, mtsogoleri wa ankhondo a mfumu anagwira Ayuda 745 kupita ku ukapolo. Onse pamodzi analipo anthu 4,600. Onani mutuwo |