Yeremiya 52:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo pambali pake panali makangaza makumi asanu ndi anai kudza asanu ndi limodzi; ndipo makangaza onse anali zana limodzi pamade pozungulira pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo pambali pake panali makangaza makumi asanu ndi anai kudza asanu ndi limodzi; ndipo makangaza onse anali zana limodzi pamade pozungulira pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Makangaza 96 anali pambali, koma onse pamodzi analipo zana limodzi, kuzungulira ukonde wonsewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Mʼmbali mwake munali makangadza 96; makangadza onse pamodzi analipo 100 kuzungulira ukonde onse. Onani mutuwo |