Yeremiya 52:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo korona wamkuwa anali pamwamba pake; utali wake wa korona mmodzi unali wa mikono isanu, ndi sefa ndi makangaza pakorona pozungulira pake, onse amkuwa: nsanamira inzake yomwe inali nazo zonga zomwezi, ndi makangaza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo korona wamkuwa anali pamwamba pake; utali wake wa korona mmodzi unali wa mikono isanu, ndi sefa ndi makangaza pakorona pozungulira pake, onse amkuwa: nsanamira inzake yomwe inali nazo zonga zomwezi, ndi makangaza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Inali ndi mutu wamkuŵa, kutalika kwake mamita aŵiri. Pozungulira mutuwo panali ukonde ndi makangaza, zonsezo zamkuŵa. Nsanamira inayo inalinso ndi makangaza ndipo inkafanana ndi inzakeyo pa zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pamwamba pa nsanamira iliyonse panali mutu wamkuwa umene kutalika kwake kunali mamita awiri. Pozungulira pake panali ukonde ndi makangadza, zonsezo za mkuwa. Nsanamira inayo inalinso ndi makangadza ake ndipo inali yofanana ndi inzake ija. Onani mutuwo |