Yeremiya 52:17 - Buku Lopatulika17 Ndi mizati yamkuwa imene inali m'nyumba ya Yehova, ndi zoikapo ndi thawale lamkuwa zimene zinali m'nyumba ya Yehova, Ababiloni anazithyolathyola, nanka nao mkuwa wake wonse ku Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndi mizati yamkuwa imene inali m'nyumba ya Yehova, ndi zoikapo ndi thawale lamkuwa zimene zinali m'nyumba ya Yehova, Ababiloni anazithyolathyola, nanka nao mkuwa wake wonse ku Babiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ankhondo a ku Babiloni adaphwanya nsanamira zamkuŵa za m'Nyumba ya Chauta, ndiponso maphaka ndi chimbiya chamkuŵa, ndipo adatenga mkuŵa wonsewo, napita nawo ku Babiloni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ababuloni anaphwanya nsanamira za mkuwa, maphaka ndi chimbiya chamkuwa zimene zinali mʼNyumba ya Yehova. Anatenga mkuwa wonsewo nʼkupita nazo ku Babuloni. Onani mutuwo |