Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 52:16 - Buku Lopatulika

16 Koma Nebuzaradani kapitao wa alonda anasiya aumphawi a padziko akhale akulima mphesa ndi akulima m'minda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma Nebuzaradani kapitao wa alonda anasiya aumphawi a padziko akhale akulima mphesa ndi akulima m'minda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma Nebuzaradani adasiyako anthu ena osauka kwambiri am'dzikomo, kuti azilima minda ya mphesa ndi minda ina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Komabe Nebuzaradani mtsogoleri wa ankhondo anasiya anthu ena onse osaukitsitsa a mʼdzikomo kuti azigwira ntchito mʼminda ya mpesa ndi minda ina.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 52:16
6 Mawu Ofanana  

Koma mkulu wa olindirira anasiya osaukadi a m'dziko akhale osunga minda yampesa, ndi alimi.


Ndipo mwezi wachisanu, tsiku lachisanu ndi chiwiri la mweziwo, ndicho chaka chakhumi mphambu chisanu ndi chinai cha mfumu Nebukadinezara mfumu ya Babiloni, Nebuzaradani mkulu wa olindirira, ndiye mnyamata wa mfumu ya Babiloni, anadza ku Yerusalemu,


Ndipo kapitao wa alonda anatenga Yeremiya, nati kwa iye, Yehova Mulungu wako ananenera choipa ichi malo ano;


Wobadwa ndi munthu iwe, iwo okhala kumabwinja a dziko la Israele anena, ndi kuti, Abrahamu anali yekha, nakhala nalo dziko cholowa chake; koma ife ndife ambiri, dzikoli lipatsidwa kwa ife cholowa chathu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa