Yeremiya 52:16 - Buku Lopatulika16 Koma Nebuzaradani kapitao wa alonda anasiya aumphawi a padziko akhale akulima mphesa ndi akulima m'minda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma Nebuzaradani kapitao wa alonda anasiya aumphawi a padziko akhale akulima mphesa ndi akulima m'minda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Nebuzaradani adasiyako anthu ena osauka kwambiri am'dzikomo, kuti azilima minda ya mphesa ndi minda ina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Komabe Nebuzaradani mtsogoleri wa ankhondo anasiya anthu ena onse osaukitsitsa a mʼdzikomo kuti azigwira ntchito mʼminda ya mpesa ndi minda ina. Onani mutuwo |