Yeremiya 52:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo mfumu ya ku Babiloni inapha ana a Zedekiya pamaso pake; niphanso akulu onse a Yuda mu Ribula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo mfumu ya ku Babiloni inapha ana a Zedekiya pamaso pake; niphanso akulu onse a Yuda m'Ribula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pompo adapha ana a Zedekiya iyeyo akupenya. Adaphanso akalonga onse a ku Yuda ku Ribula komweko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ku Ribulako mfumu ya ku Babuloni inapha ana aamuna a Zedekiya iyeyo akuona; ndiponso inapha akuluakulu onse a ku Yuda. Onani mutuwo |