Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 51:61 - Buku Lopatulika

61 Ndipo Yeremiya anati kwa Seraya, Pamene ufika ku Babiloni, samalira kuti uwerenge mau awa onse,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

61 Ndipo Yeremiya anati kwa Seraya, Pamene ufika ku Babiloni, samalira kuti uwerenge mau awa onse,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

61 Yeremiyayo adauza Seraya kuti, “Pamene ukafike ku Babiloni, usakalephere kuŵaŵerengera anthu mau onseŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

61 Yeremiya anawuza Seraya kuti, “Ukakafika ku Babuloni, ukaonetsetse kuti wawawerengera anthu onse mawu onsewa.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 51:61
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yeremiya analemba m'buku choipa chonse chimene chidzafika pa Babiloni, mau onse awa olembedwa za Babiloni.


nuti, Inu Yehova, mwanena za malo ano, kuti mudzawatha, kuti asakhalemo, ngakhale anthu ngakhale nyama, koma akhale bwinja nthawi za nthawi.


Ndipo Yesu anatuluka ku Kachisi; ndipo ophunzira ake anadza kudzamuonetsa chimangidwe cha Kachisiyo.


Ndipo pamene analikutuluka Iye mu Kachisi, mmodzi wa ophunzira ake ananena kwa Iye, Mphunzitsi, onani, miyala yotere ndi nyumba yotere.


Ndipo pamene mudamwerenga kalata iyi, amwerengenso mu Mpingo wa ku Laodikea, ndi inunso muwerenge wa ku Laodikea.


Chomwecho, tonthozanani ndi mau awa.


Ndikulumbirirani pa Ambuye kuti kalatayi iwerengedwe kwa abale onse.


Wodala iye amene awerenga, ndi iwo amene akumva mau a chinenerocho, nasunga zolembedwa momwemo; pakuti nthawi yayandikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa