Yeremiya 51:6 - Buku Lopatulika6 Thawani pakati pa Babiloni, yense apulumuke moyo wake; musathedwe m'choipa chake; pakuti ndi nthawi ya kubwezera chilango; Yehova adzambwezera iye mphotho yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Thawani pakati pa Babiloni, yense apulumuke moyo wake; musathedwe m'choipa chake; pakuti ndi nthawi ya kubwezera chilango; Yehova adzambwezera iye mphotho yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Aliyense mwa inu athaŵe, achoke ku Babiloni kuti apulumutse moyo wake. Musaphedwe naye pamodzi pamene adzalandira chilango chake. Limeneli ndilodi tsiku limene Chauta adzaŵalanga, ndipo adzaŵalipsira kwathunthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Thawaniko ku Babuloni! Aliyense apulumutse moyo wake! Musawonongeke naye pamodzi chifukwa cha machimo ake. Imeneyi ndi nthawi yoti Yehova amulange; Yehova adzamulipsira. Onani mutuwo |