Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 51:54 - Buku Lopatulika

54 Mau akufuula ochokera ku Babiloni, ndi a chionongeko chachikulu ku dziko la Ababiloni!

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Mau akufuula ochokera ku Babiloni, ndi a chionongeko chachikulu ku dziko la Ababiloni!

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 “Imvani mau olira m'Babiloni. Imvani phokoso la kuwonongeka kwakukulu m'dziko la Ababiloni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 “Imvani mfuwu wolira kuchokera ku Babuloni. Imvani phokoso lachiwonongeko chachikulu kuchokera mʼdziko la Babuloni.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 51:54
10 Mawu Ofanana  

Mtima wanga ufuula chifukwa cha Mowabu: akulu ake athawira ku Zowari, ku Egilati-Selisiya; pakuti pa chikweza cha Luhiti akwera alikulira, pakuti m'njira ya Horonaimu akweza mfuu wa chionongeko.


Monga kutentha m'malo ouma, Inu mudzaletsa phokoso la alendo; nyimbo ya akuopsa idzaletseka, monga mthunzi uletsa dzuwa.


Phokoso la nkhondo lili m'dziko lino, ndi lakuononga kwakukulu.


Iphani ng'ombe zamphongo zake zonse; zitsikire kukaphedwa; tsoka iwo! Pakuti tsiku lao lafika, tsiku la kulanga kwao.


Mfumu ya ku Babiloni yamva mbiri yao, ndipo manja ake alefuka; wagwidwa ndi nkhawa, ndi zowawa zonga za mkazi alimkudwala.


Dziko lapansi linthunthumira, pa phokoso la kugwidwa kwa Babiloni, ndipo mfuu wamveka mwa amitundu.


Ndipo tsiku ilo, ati Yehova, kudzakhala phokoso lakulira lochokera ku Chipata cha Nsomba, ndi kuchema kochokera kudera lachiwiri, ndi kugamuka kwakukulu kochokera kuzitunda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa