Yeremiya 51:53 - Buku Lopatulika53 Ngakhale Babiloni adzakwera kumwamba, ngakhale adzalimbitsa msanje wa mphamvu yake, koma kuchokera kwa Ine akufunkha adzafika kwa iye, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Ngakhale Babiloni adzakwera kumwamba, ngakhale adzalimbitsa msanje wa mphamvu yake, koma kuchokera kwa Ine akufunkha adzafika kwa iye, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Ngakhale Babiloni adzikweze mpaka ku mlengalenga, nkulimbitsa nsanja zake, ndidzatuma oononga kuti amgonjetse,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Ngakhale Babuloni atadzikweza mpaka mlengalenga ndi kulimbitsa nsanja zake, ndidzatuma anthu owononga kudzamenyana naye,” akutero Yehova. Onani mutuwo |