Yeremiya 51:52 - Buku Lopatulika52 Chifukwa chake, taona, masiku alinkudza, ati Yehova, amene ndidzaweruza mafano ake; ndipo padziko lake lonse olasidwa adzabuula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Chifukwa chake, taona, masiku alinkudza, ati Yehova, amene ndidzaweruza mafano ake; ndipo pa dziko lake lonse olasidwa adzabuula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Koma Chauta akunena kuti, “Ikubwera nthaŵi pamene ndidzalange mafano a ku Babiloni, ndipo kubuula kwa anthu olasidwa kudzamveka m'dziko lake lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Nʼchifukwa chake Yehova akuti, “Masiku akubwera pamene ndidzalanga mafano ake, ndipo mʼdziko lake lonse anthu ovulala adzabuwula. Onani mutuwo |