Yeremiya 51:51 - Buku Lopatulika51 Tili ndi manyazi, chifukwa tamva mnyozo; manyazi aphimba nkhope zathu; pakuti alendo alowa m'malo opatulika a nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Tili ndi manyazi, chifukwa tamva mnyozo; manyazi aphimba nkhope zathu; pakuti alendo alowa m'malo opatulika a nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Inu mukuti ‘Tikuchita manyazi chifukwa cha manyozo amene talandira. Nkhope zathu zagwa chifukwa anthu achilendo aloŵa ku mabwalo opatulika a ku Nyumba ya Chauta.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Inu mukuti, “Tikuchita manyazi, chifukwa tanyozedwa ndipo nkhope zathu zili ndi manyazi, chifukwa anthu achilendo alowa malo opatulika a Nyumba ya Yehova.” Onani mutuwo |