Yeremiya 51:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti Israele ndi Yuda sasiyidwa ndi Mulungu wao, ndiye Yehova wa makamu: ngakhale dziko lao ladzala ndi uchimo kuchimwira Woyera wa Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti Israele ndi Yuda sasiyidwa ndi Mulungu wao, ndiye Yehova wa makamu: ngakhale dziko lao ladzala ndi uchimo kuchimwira Woyera wa Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Israele ndi Yuda sadasiyidwe ndi Mulungu wao, Chauta Wamphamvuzonse. Koma dziko la Ababiloni nlodzaza ndi machimo, machimo ake onyoza Woyera uja wa Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pakuti Yuda ndi Israeli sanasiyidwe ngati amasiye ndi Mulungu wawo, Yehova Wamphamvuzonse, koma ngakhale dziko la Babuloni ndi lodzaza ndi machimo pamaso pa Woyerayo wa Israeli. Onani mutuwo |