Yeremiya 51:47 - Buku Lopatulika47 Chifukwa chake, taonani, masiku alinkudza, amene ndidzaweruza mafano osemasema a Babiloni, ndipo dziko lake lonse lidzakhala ndi manyazi; ndipo ophedwa ake onse adzagwa pakati pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Chifukwa chake, taonani, masiku alinkudza, amene ndidzaweruza mafano osemasema a Babiloni, ndipo dziko lake lonse lidzakhala ndi manyazi; ndipo ophedwa ake onse adzagwa pakati pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 “Tsono ikudza nthaŵi pamene ndidzalange mafano a Babiloni. Dziko lonselo lidzachita manyazi. Anthu ake onse ophedwa adzakhala ali ngundangunda pakati pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Pakuti taonani, nthawi ikubwera ndithu pamene ndidzalanga mafano a ku Babuloni; dziko lake lonse lidzachita manyazi ndi ophedwa ake onse adzakhala ngundangunda pakati pake. Onani mutuwo |