Yeremiya 51:44 - Buku Lopatulika44 Ndipo Ine ndiweruza Beli mu Babiloni, ndipo ndidzatulutsa m'kamwa mwake chomwe wachimeza; ndipo amitundu sadzasonkhaniranso konse kwa iye; inde, khoma la Babiloni lidzagwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Ndipo Ine ndiweruza Beli m'Babiloni, ndipo ndidzatulutsa m'kamwa mwake chomwe wachimeza; ndipo amitundu sadzasonkhaniranso konse kwa iye; inde, khoma la Babiloni lidzagwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Ndidzalanga Beli, mulungu wa Ababiloni, ndidzamsanzitsa zimene adameza. Mitundu ya anthu sidzapitanso kwa iye. Malinga a Babiloni agwa! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Ndidzalanga Beli mulungu wa Ababuloni, ndidzamusanzitsa zimene anameza. Mitundu ya anthu sidzapitanso kwa iye. Malinga a Babuloni agwa. Onani mutuwo |