Yeremiya 51:41 - Buku Lopatulika41 Sesaki wagwidwatu! Chimene dziko lonse lapansi linachitamanda chalandidwa dzidzidzi! Babiloni wakhalatu bwinja pakati pa amitundu! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Sesaki wagwidwatu! Chimene dziko lonse lapansi linachitamanda chalandidwa dzidzidzi! Babiloni wakhalatu bwinja pakati pa amitundu! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 “Ndithu Babiloni wagonjetsedwa, mzinda umene dziko lonse lapansi linkaunyadira walandidwa. Ogo! Babiloni uja wasanduka chinthu chonyansa pakati pa mitundu ya anthu! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 “Ndithu Babuloni walandidwa, mzinda umene dziko lonse lapansi limanyadira wagwidwa! Taonani, mmene Babuloni wasandukira chinthu chochititsa mantha pakati pa mitundu ya anthu! Onani mutuwo |