Yeremiya 51:40 - Buku Lopatulika40 Ndidzawagwetsa kuti aphedwe monga anaankhosa amphongo, ndi atonde. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndidzawagwetsa kuti aphedwe monga anaankhosa amphongo, ndi atonde. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Ndidzapita nawo kuti akaphedwe ngati anaankhosa, ngati nkhosa zamphongo kapena atonde,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 “Ine ndidzawatenga kuti akaphedwe ngati ana ankhosa onenepa, ngati nkhosa zazimuna ndi mbuzi. Onani mutuwo |