Yeremiya 51:34 - Buku Lopatulika34 Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni wandidya ine, wandiphwanya ine, wandiyesa ine ngati mbiya yopanda kanthu, wandimeza ngati ng'ona, wadzaza m'kamwa mwake ndi zotsekemera zanga, wanditaya ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni wandidya ine, wandiphwanya ine, wandiyesa ine ngati mbiya yopanda kanthu, wandimeza ngati ng'ona, wadzaza m'kamwa mwake ndi zotsekemera zanga, wanditaya ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 A ku Yerusalemu akuti, “Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, watiwononga, Watitswanya ndi kutitaya ngati mbiya yopanda kanthu. Watimeza ngati ng'ona. Wakhuta ndi zakudya zathu zotsekemera, kenaka nkutilavula.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 A ku Yerusalemu akuti, “Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni watiwononga, watiphwanya, ndi kutitaya ngati mbiya yopanda kanthu. Watimeza ngati ngʼona, wakhuta ndi zakudya zathu zokoma, kenaka nʼkutilavula.” Onani mutuwo |