Yeremiya 51:30 - Buku Lopatulika30 Olimba a ku Babiloni akana kumenyana, akhala m'malinga ao; mphamvu yao yalephera; akhala ngati akazi; nyumba zake zapsa ndi moto; akapichi ake athyoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Olimba a ku Babiloni akana kumenyana, akhala m'malinga ao; mphamvu yao yalephera; akhala ngati akazi; nyumba zake zapsa ndi moto; akapichi ake athyoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ankhondo a ku Babiloni aleka kuponya nkhondo, angokhala khale m'malinga ao. Mphamvu zao zatha, asanduka ngati akazi. Nyumba zake zatenthedwa, mipiringidzo ya zipata zake yathyoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ankhondo a ku Babuloni aleka kuchita nkhondo; iwo angokhala mʼmalinga awo. Mphamvu zawo zatheratu; ndipo akhala ngati akazi. Malo ake wokhala atenthedwa; mipiringidzo ya zipata zake yathyoka. Onani mutuwo |