Yeremiya 51:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo sadzachotsa pa iwe mwala wa pangodya, kapena mwala wa pamaziko; koma udzakhala bwinja nthawi zonse, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo sadzachotsa pa iwe mwala wa pangodya, kapena mwala wa pamaziko; koma udzakhala bwinja nthawi zonse, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Palibe mwala wako ndi umodzi womwe umene adzabwere nawo kuti augwiritse ntchito ngati mwala wapangodya. Iwe udzakhala chipululu mpaka muyaya,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Palibe ngakhale ndi mwala wako umodzi umene anthu adzawutenga kuti awugwiritse ntchito kumangira nyumba, chifukwa iwe udzakhala chipululu mpaka muyaya,” akutero Yehova. Onani mutuwo |