Yeremiya 51:21 - Buku Lopatulika21 ndi iwe ndidzathyolathyola kavalo ndi wokwera wake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndi iwe ndidzathyolathyola kavalo ndi wokwera wake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndi iwe ndimaphwanyaphwanya akavalo ndi okwerapo ao. Ndi iwe ndimaphwanyaphwanya magaleta ndi oyendetsa ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 ndi iwe ndimaphwanya kavalo ndi wokwerapo, ndi iwe ndimaphwanya galeta ndi woyendetsa wake. Onani mutuwo |