Yeremiya 51:18 - Buku Lopatulika18 Ngwachabe, chiphamaso; nthawi ya kulangidwa kwao adzatayika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ngwachabe, chiphamaso; nthawi ya kulangidwa kwao adzatayika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mafanowo ngachabechabe, oyenera kuŵaseka, ndipo pamene anthuwo adzalangidwe, mafanowo adzaonongedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mafanowo ndi achabechabe, zinthu zosekedwa nazo. Pamene anthuwo azidzaweruzidwa mafanowo adzawonongedwa. Onani mutuwo |