Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 51:17 - Buku Lopatulika

17 Anthu onse ali opulukira ndi opanda nzeru; wakusula golide achitidwa manyazi ndi fanizo lake losema; pakuti fanizo lake loyenga lili bodza, mulibe mpweya m'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Anthu onse ali opulukira ndi opanda nzeru; wakusula golide achitidwa manyazi ndi fanizo lake losema; pakuti fanizo lake loyenga lili bodza, mulibe mpweya m'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Anthu onse ndi opusa, alibe nzeru. Mmisiri aliyense wosula amachita manyazi ndi mafano ake. Mafano amene amapangawo ngabodza, mwa iwo mulibe konse moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 “Anthu onse ndi opusa ndiponso opanda nzeru; mmisiri aliyense wosula golide akuchita manyazi ndi mafano ake. Mafano akewo ndi abodza; alibe moyo mʼkati mwawo.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 51:17
12 Mawu Ofanana  

Pakamwa ali napo, koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;


Adzafanana nao iwo akuwapanga; ndi onse akuwakhulupirira.


Yehova mu Mwamba anaweramira pa ana a anthu, kuti aone ngati aliko wanzeru, wakufuna Mulungu.


Anthu onse ali opulukira ndi opanda nzeru; woyenga yense anyazitsidwa ndi fanizo lake losemasema; pakuti fanizo lake loyenga lili bodza, mulibe mpweya mwa iwo.


Lalikirani mwa amitundu, falikitsani, kwezani mbendera; falikitsani, musabise; munene, Babiloni wagwidwa, Beli wachitidwa manyazi, Merodaki wathyokathyoka, zosema zake zachitidwa manyazi, mafano ake athyokathyoka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa