Yeremiya 51:14 - Buku Lopatulika14 Yehova wa makamu walumbira pa Iye mwini, kuti, Ndithu ndidzakudzaza iwe ndi anthu, monga ndi madzombe; ndipo adzakukwezera iwe mfuu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Yehova wa makamu walumbira pa Iye mwini, kuti, Ndithu ndidzakudzaza iwe ndi anthu, monga ndi madzombe; ndipo adzakukwezera iwe mfuu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chauta Wamphamvuzonse adalumbira pali Iye yemwe mwini wake kuti, “Ndidzatuma anthu osaŵerengeka ngati dzombe kuti adzakuthireni nkhondo, ndipo adzafuula, kuwonetsa kuti apambana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yehova Wamphamvuzonse analumbira pali Iye mwini kuti: Ndidzakutumizira adani ochuluka ngati dzombe, kuti adzakuthire nkhondo ndipo adzafuwula kuonetsa kuti apambana. Onani mutuwo |