Yeremiya 51:13 - Buku Lopatulika13 Iwe wokhala pamadzi ambiri, wochuluka chuma, chimaliziro chako chafika, chilekezero cha kusirira kwako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Iwe wokhala pa madzi ambiri, wochuluka chuma, chimaliziro chako chafika, chilekezero cha kusirira kwako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Inu amene muli ndi mitsinje yambiri, ndinu olemera kwambiri, koma chimalizo chanu chafika, moyo wanu watha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Inu muli ndi mitsinje yambiri ndi chuma chambiri. Koma chimaliziro chanu chafika, moyo wanu watha. Onani mutuwo |