Yeremiya 51:12 - Buku Lopatulika12 Muwakwezere mbendera makoma a Babiloni, mulimbikitse ulonda, muike alonda, mupangiretu olalira, pakuti Yehova waganiziratu ndi kuchita chomwe ananena za okhala mu Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Muwakwezere mbendera makoma a Babiloni, mulimbikitse ulonda, muike alonda, mupangiretu olalira, pakuti Yehova waganiziratu ndi kuchita chomwe ananena za okhala m'Babiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kwezani mbendera yankhondo ndipo muwononge malinga a Babiloni. Mulimbitse oteteza, muike alonda, mukonzekere kulalira. Pakuti Chauta watsimikiza, ndipo adzachitadi zimene adanena za anthu a ku Babiloni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kwezani mbendera yankhondo kuti muwononge malinga a Babuloni! Limbitsani oteteza, ikani alonda pa malo awo, konzekerani kulalira. Pakuti Yehova watsimikiza ndipo adzachitadi zomwe ananena za anthu a ku Babuloni. Onani mutuwo |