Yeremiya 50:8 - Buku Lopatulika8 Thawani pakati pa Babiloni, tulukani m'dziko la Ababiloni, mukhale monga atonde patsogolo pa zoweta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Thawani pakati pa Babiloni, tulukani m'dziko la Ababiloni, mukhale monga atonde patsogolo pa zoweta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Thaŵaniko ku Babiloni. Chokaniko ku dziko la Ababiloni, muyambe ndinu kutuluka, ngati atonde otsogolera ziŵeto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Thawaniko ku Babuloni; chokani mʼdziko la Ababuloni. Muyambe inu kutuluka ngati atonde amene amatsogolera ziweto. Onani mutuwo |