Yeremiya 50:5 - Buku Lopatulika5 Adzafunsira Ziyoni nkhope zao zilikuyang'ana kumeneko, ndi kuti, Tiyeni inu, dzilumikizeni kwa Yehova m'chipangano cha muyaya chimene sichidzaiwalika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Adzafunsira Ziyoni nkhope zao zilikuyang'ana kumeneko, ndi kuti, Tiyeni inu, dzilumikizeni kwa Yehova m'chipangano cha muyaya chimene sichidzaiwalika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adzafunsa njira ya ku Ziyoni, nkuyamba ulendo wobwerera kumeneko. Adzati, ‘Tiyeni tibwerere kwa Chauta, tikachite naye chipangano chamuyaya, chimene sichidzaiŵalika konse.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Adzafunsa njira ya ku Ziyoni ndi kuyamba ulendo wopita kumeneko. Iwo adzadzipereka kwa Yehova pochita naye pangano lamuyaya limene silidzayiwalika. Onani mutuwo |