Yeremiya 50:41 - Buku Lopatulika41 Taonani, anthu achokera kumpoto; ndiwo mtundu waukulu, ndipo maufumu ambiri adzaukitsidwa kuchokera ku malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Taonani, anthu achokera kumpoto; ndiwo mtundu waukulu, ndipo maufumu ambiri adzaukitsidwa kuchokera ku malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 “Onani, ankhondo akubwera kuchokera kumpoto. Anthu a mtundu wanyonga ndi mafumu ambiri akunyamuka kuchokera ku madera akutali a dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 “Taonani! Gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto; mtundu wa anthu amphamvu pamodzi ndi mafumu ambiri, wanyamuka kuchokera kumathero a dziko lapansi. Onani mutuwo |