Yeremiya 50:4 - Buku Lopatulika4 Masiku omwewo, nthawi yomweyo, ati Yehova, ana a Israele adzadza, iwo ndi ana a Yuda; pamodzi adzayenda m'njira mwao alinkulira, nadzafuna Yehova Mulungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Masiku omwewo, nthawi yomweyo, ati Yehova, ana a Israele adzadza, iwo ndi ana a Yuda; pamodzi adzayenda m'njira mwao alinkulira, nadzafuna Yehova Mulungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta akunena kuti, “Masiku amenewo, nthaŵi imeneyo Aisraele ndi Ayuda adzasonkhana pamodzi, azikabwera nalira. Adzafunitsitsa kuchita zimene Chauta Mulungu wao afuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Masiku amenewo, nthawi imeneyo,” akutero Yehova, “anthu a ku Israeli ndi anthu a ku Yuda onse pamodzi adzabwera akulira. Adzafunitsitsa kuchita zimene Yehova Mulungu wawo akufuna. Onani mutuwo |