Yeremiya 50:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti mtundu wa anthu udzatuluka kumpoto kudzamenyana naye, udzachititsa dziko lake bwinja, losakhalamo anthu; athawa, apita, anthu ndi nyama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti mtundu wa anthu udzatuluka kumpoto kudzamenyana naye, udzachititsa dziko lake bwinja, losakhalamo anthu; athawa, apita, anthu ndi nyama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Mtundu wa anthu akumpoto wadzauthira nkhondo mzinda wa Babiloni. Dziko lake adzalisandutsa bwinja, ndipo kumeneko sikudzakhalanso munthu kapena nyama.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mtundu wa anthu wochokera kumpoto wadzathira nkhondo Babuloni ndi kusandutsa bwinja dziko lake. Kumeneko sikudzakhalanso munthu kapena nyama. Onani mutuwo |