Yeremiya 50:2 - Buku Lopatulika2 Lalikirani mwa amitundu, falikitsani, kwezani mbendera; falikitsani, musabise; munene, Babiloni wagwidwa, Beli wachitidwa manyazi, Merodaki wathyokathyoka, zosema zake zachitidwa manyazi, mafano ake athyokathyoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Lalikirani mwa amitundu, falikitsani, kwezani mbendera; falikitsani, musabise; munene, Babiloni wagwidwa, Beli wachitidwa manyazi, Merodaki wathyokathyoka, zosema zake zachitidwa manyazi, mafano ake athyokathyoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Ulengeze ndi kulalika kwa anthu a mitundu yonse. Kweza mbendera ndipo usabise kanthu, uŵauze kuti, ‘Babiloni wagwa! Mulungu wake Beli wachititsidwa manyazi, nayenso Merodaki wataya mtima. Mafano ake anyozedwa kwambiri, milungu yake yataya mtima.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Lengeza ndi kulalika pakati pa anthu a mitundu ina, kweza mbendera ndipo ulengeze; usabise kanthu, koma uwawuze kuti, ‘Babuloni wagwa; mulungu wawo Beli wachititsidwa manyazi, nayenso Mariduku wagwidwa ndi mantha. Milungu yake yagwidwa ndi mantha ndipo mafano ake adzagwidwa ndi mantha.’ Onani mutuwo |