Yeremiya 50:1 - Buku Lopatulika1 Mau amene ananena Yehova za Babiloni, za dziko la Ababiloni, mwa Yeremiya mneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau amene ananena Yehova za Babiloni, za dziko la Ababiloni, mwa Yeremiya mneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Naŵa mau amene Chauta adalankhula ndi mneneri Yeremiya kunena za mzinda wa Babiloni ndi anthu ake. Adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uthenga umene Yehova anayankhula ndi mneneri Yeremiya wonena za mzinda wa Babuloni ndi anthu ake ndi uwu: Onani mutuwo |