Yeremiya 5:30 - Buku Lopatulika30 Chodabwitsa ndi choopsa chaoneka m'dzikomo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Chodabwitsa ndi choopsa chaoneka m'dzikomo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 M'dziko muno mwachitika chinthu chododometsa ndi choopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Chinthu chothetsa nzeru ndi choopsa kwambiri chachitika mʼdzikomo: Onani mutuwo |