Yeremiya 5:29 - Buku Lopatulika29 Sindidzawalanga kodi chifukwa cha zimenezi? Ati Yehova; kodi moyo wanga sudzabwezera chilango mtundu wotere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Sindidzawalanga kodi chifukwa cha zimenezi? Ati Yehova; kodi moyo wanga sudzabwezera chilango mtundu wotere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Chauta akuti, “Ndiye ndingapande kuŵalanga chifukwa cha zimenezi? Monga ndisaulipsire mtundu wochita zotere?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Kodi Ine ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi? Kodi ndisawulipsire mtundu woterewu? Akutero Yehova. Onani mutuwo |