Yeremiya 5:27 - Buku Lopatulika27 Monga chikwere chodzala ndi mbalame, chomwecho nyumba zao zadzala ndi chinyengo; chifukwa chake akula, alemera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Monga chikwere chodzala ndi mbalame, chomwecho nyumba zao zadzala ndi chinyengo; chifukwa chake akula, alemera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Nyumba zao nzodzaza ndi chuma chochipeza mwachinyengo, ngati chitatanga chodzaza ndi mbalame. Nchifukwa chake adasanduka otchuka ndi olemera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nyumba zawo zadzaza ndi chuma chochipeza mwa chinyengo ngati zikwere zodzaza ndi mbalame. Nʼchifukwa chake asanduka otchuka ndi olemera. Onani mutuwo |