Yeremiya 5:26 - Buku Lopatulika26 Pakuti mwa anthu anga aoneka anthu oipa; adikira monga akutcha misampha; atcha khwekhwe, agwira anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pakuti mwa anthu anga aoneka anthu oipa; adikira monga akucha misampha; acha khwekhwe, agwira anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Paja mwa anthu anga muli ena achifwamba, amene amalalira anzao monga m'mene amachitira otchera mbalame. Amatcha misampha nakola anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “Pakati pa anthu anga pali anthu ena oyipa amene amabisalira anzawo monga amachitira mlenje mbalame ndiponso ngati amene amatchera misampha kuti akole anthu anzawo. Onani mutuwo |